Masalimo 73:26 - Buku Lopatulika26 Likatha thupi langa ndi mtima wanga, Mulungu ndiye thanthwe la mtima wanga, ndi cholandira changa chosatha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Likatha thupi langa ndi mtima wanga, Mulungu ndiye thanthwe la mtima wanga, ndi cholandira changa chosatha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Thupi langa ndi mtima wanga zingafooke chotani, Mulungu ndiye mphamvu za mtima wanga ndiyenso wondigaŵira madalitso mpaka muyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Thupi ndi mtima wanga zitha kufowoka, koma Mulungu ndiye mphamvu ya mtima wanga ndi cholandira changa kwamuyaya. Onani mutuwo |