Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 73:23 - Buku Lopatulika

23 Koma ndikhala ndi Inu chikhalire, mwandigwira dzanja langa la manja.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Koma ndikhala ndi Inu chikhalire, mwandigwira dzanja langa la manja.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Koma chonsecho ndili ndi Inu nthaŵi zonse. Inu mumandigwira dzanja lamanja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Komabe ineyo ndili ndi Inu nthawi zonse; mumandigwira dzanja langa lamanja.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 73:23
14 Mawu Ofanana  

Pamene Abramu anali wa zaka makumi asanu ndi anai kudza zisanu ndi zinai, Yehova anamuonekera Abramu nati kwa iye, Ine ndine Mulungu Wamphamvuyonse; yenda iwe pamaso panga, nukhale wangwiro.


Ndikaziwerenga zichuluka koposa mchenga: Ndikauka ndikhalanso nanu.


Ndaika Yehova patsogolo panga nthawi zonse; popeza ali padzanja langa lamanja, sindidzagwedezeka.


Inde, ndingakhale ndiyenda m'chigwa cha mthunzi wa imfa, sindidzaopa choipa; pakuti Inu muli ndi ine; chibonga chanu ndi ndodo yanu, izi zindisangalatsa ine.


Pakuti manja a oipa adzathyoledwa, koma Yehova achirikiza olungama.


Angakhale akagwa, satayikiratu, pakuti Yehova agwira dzanja lake.


Moyo wanga uumirira Inu. Dzanja lamanja lanu lindigwiriziza.


usaope, pakuti Ine ndili pamodzi ndi iwe; usaopsedwe, pakuti Ine ndine Mulungu wako; ndidzakulimbitsa; inde, ndidzakuthangata; inde, ndidzakuchirikiza ndi dzanja langa lamanja la chilungamo.


Pakuti Ine Yehova Mulungu wako ndidzagwira dzanja lako lamanja, ndi kunena kwa iwe, Usaope ndidzakuthandiza iwe.


Taona Mtumiki wanga, amene ndimgwiriziza; Wosankhika wanga, amene moyo wanga ukondwera naye; ndaika mzimu wanga pa Iye; Iye adzatulutsira amitundu chiweruziro.


Onani namwali adzaima, nadzabala mwana wamwamuna, ndipo adzamutcha dzina lake, Imanuele. Ndilo losandulika, Mulungu nafe.


ndi kuwaphunzitsa, asunge zinthu zonse zimene ndinakulamulani inu; ndipo onani, Ine ndili pamodzi ndi inu masiku onse, kufikira chimaliziro cha nthawi ya pansi pano.


Mtima wanu ukhale wosakonda chuma; zimene muli nazo zikukwanireni; pakuti Iye anati, Sindidzakusiya konse, kungakhale kukutaya, sindidzakutaya ndithu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa