Masalimo 71:8 - Buku Lopatulika8 M'kamwa mwanga mudzadzala lemekezo lanu, ndi ulemu wanu tsiku lonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 M'kamwa mwanga mudzadzala lemekezo lanu, ndi ulemu wanu tsiku lonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Pakamwa panga pakutamanda Inu, pakulalika ulemerero wanu tsiku lonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Pakamwa panga padzaza ndi matamando anu, kulengeza ulemerero wanu tsiku lonse. Onani mutuwo |