Masalimo 71:23 - Buku Lopatulika23 Milomo yanga idzafuula mokondwera poimbira Inu nyimbo; inde, moyo wanga umene munaombola. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Milomo yanga idzafuula mokondwera poimbira Inu nyimbo; inde, moyo wanga umene munaombola. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Pakamwa panga padzafuula ndi chimwemwe, pamene ndikukuimbirani nyimbo zotamanda. Nawonso mtima wanga umene mwauwombola, udzaimba moyamika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Milomo yanga idzafuwula ndi chimwemwe pamene ndidzayimba matamando kwa Inu amene mwandiwombola. Onani mutuwo |