Masalimo 71:15 - Buku Lopatulika15 Pakamwa panga padzafotokozera chilungamo chanu, ndi chipulumutso chanu tsiku lonse; pakuti sindidziwa mawerengedwe ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Pakamwa panga padzafotokozera chilungamo chanu, ndi chipulumutso chanu tsiku lonse; pakuti sindidziwa mawerengedwe ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Pakamwa panga padzalankhula tsiku lonse za ntchito zanu zolungama ndi za chipulumutso chanu, popeza kuti sindidziŵa chiŵerengero chake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Pakamwa panga padzafotokoza za chilungamo chanu, za chipulumutso chanu tsiku lonse, ngakhale sindikudziwa muyeso wake. Onani mutuwo |