Masalimo 7:9 - Buku Lopatulika9 Ithe mphulupulu ya anthu oipa, ndikupemphani, koma wolungamayo mumkhazikitse. Pakuti woyesa mitima ndi impso ndiye Mulungu wolungama. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ithe mphulupulu ya anthu oipa, ndikupemphani, koma wolungamayo mumkhazikitse. Pakuti woyesa mitima ndi impso ndiye Mulungu wolungama. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Thetsani ntchito zoipa za anthu ochimwa, koma anthu ochita zabwino muŵabwezere zokoma. Inu ndinu amene mumayesa maganizo ndi mitima yomwe, Inu ndinu Mulungu wolungama. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Inu Mulungu wolungama, amene mumasanthula maganizo ndi mitima, thetsani chiwawa cha anthu oyipa ndipo wolungama akhale motetezedwa. Onani mutuwo |