Masalimo 7:15 - Buku Lopatulika15 Anachita dzenje, nalikumba, nagwa m'mbuna yomwe anaikumba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Anachita dzenje, nalikumba, nagwa m'mbuna yomwe anaikumba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Amakumba mbuna kuti ikhale yozama, koma amagwamo ndiye yemwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Iye amene akumba dzenje ndi kulizamitsa amagwera mʼdzenje limene wakumbalo. Onani mutuwo |