Masalimo 7:11 - Buku Lopatulika11 Mulungu ndiye Woweruza wolungama, ndiye Mulungu wakukwiya masiku onse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Mulungu ndiye Woweruza wolungama, ndiye Mulungu wakukwiya masiku onse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Mulungu ndiye muweruzi wolungama, amalanga anthu oipa nthaŵi zonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Mulungu amaweruza molungama, Mulungu amene amaonetsa ukali wake tsiku ndi tsiku. Onani mutuwo |