Masalimo 69:29 - Buku Lopatulika29 Koma ine ndine wozunzika ndi womva zowawa; chipulumutso chanu, Mulungu, chindikweze pamsanje. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Koma ine ndine wozunzika ndi womva zowawa; chipulumutso chanu, Mulungu, chindikweze pamsanje. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Koma ine ndazunzika ndipo ndikumva kuŵaŵa. Nyamuleni Inu Mulungu, kuti ndipulumuke. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Ndikumva zowawa ndi kuzunzika; lolani chipulumutso chanu, Inu Mulungu, chinditeteze. Onani mutuwo |