Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 69:12 - Buku Lopatulika

12 Okhala pachipata akamba za ine; ndipo oledzera andiimba.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Okhala pachipata akamba za ine; ndipo oledzera andiimba.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Anthu okhala pa chipata amandinena, ndipo zidakwa zimandiimba nyimbo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Iwo amene amakhala pa chipata amandinena, ndipo ine ndine nyimbo ya zidakwa.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 69:12
15 Mawu Ofanana  

Ndipo anadza ku Sodomu madzulo amithenga awiri; ndipo Loti anakhala pa chipata cha Sodomu, ndipo Loti anaona iwo, nauka kuti akakomane nao, ndipo anaweramitsa pansi nkhope yake.


Koma ine, pakudwala iwowa, chovala changa ndi chiguduli. Ndinazunza moyo wanga ndi kusala; ndipo pemphero langa linabwera kuchifuwa changa.


Yehova, mwandikopa ine, ndipo ndinakopedwa; muli ndi mphamvu koposa ine, ndipo mwapambana; ine ndikhala choseketsa dzuwa lonse, onse andiseka.


koma munadzikweza kutsutsana naye Ambuye wa Kumwamba; ndipo anabwera nazo zotengera za nyumba yake kwa inu; ndi inu ndi akulu anu, akazi anu ndi akazi anu aang'ono, mwamweramo vinyo; mwalemekezanso milungu yasiliva, ndi yagolide, yamkuwa, yachitsulo, yamtengo, ndi yamwala, imene siiona kapena kumva, kapena kudziwa; ndi Mulungu amene m'dzanja mwake muli mpweya wanu, ndi njira zanu zonse, yemweyo simunamchitire ulemu.


Koma ansembe aakulu ndi akulu anapangira anthu kuti apemphe Barabasi, koma kuti aononge Yesu.


Ndipo anayamba kumnenera Iye, kuti, Tinapeza munthu uyu alikupandutsa anthu a mtundu wathu, ndi kuwaletsa kupereka msonkho kwa Kaisara, nadzinenera kuti Iye yekha ndiye Khristu mfumu.


Mudziikire oweruza ndi akapitao m'midzi yanu yonse imene Yehova Mulungu wanu akupatsani, monga mwa mafuko anu; ndipo aweruze anthu ndi chiweruzo cholungama.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa