Masalimo 68:5 - Buku Lopatulika5 Mulungu, mokhala mwake moyera, ndiye Atate wa ana amasiye, ndi woweruza wa akazi amasiye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Mulungu, mokhala mwake moyera, ndiye Atate wa ana amasiye, ndi woweruza wa akazi amasiye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Atate a ana amasiye ndiponso mtetezi wa azimai amasiye, ndi Mulungu amene amakhala m'malo ake oyera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Atate wa ana amasiye, mtetezi wa akazi amasiye, ndiye Mulungu amene amakhala mʼmalo oyera. Onani mutuwo |