Masalimo 68:3 - Buku Lopatulika3 Koma olungama akondwere; atumphe ndi chimwemwe pamaso pa Mulungu; ndipo asekere nacho chikondwerero. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Koma olungama akondwere; atumphe ndi chimwemwe pamaso pa Mulungu; ndipo asekere nacho chikondwerero. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Koma anthu anu Mulungu, akondwere, asangalale pamaso panu, inde, asekere ndi chimwemwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Koma olungama asangalale ndi kukondwera pamaso pa Mulungu; iwo akondwere ndi kusangalala. Onani mutuwo |