Masalimo 59:1 - Buku Lopatulika1 Ndilanditseni kwa adani anga, Mulungu wanga, ndiikeni pamsanje kwa iwo akundiukira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndilanditseni kwa adani anga, Mulungu wanga, ndiikeni pamsanje kwa iwo akundiukira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Pulumutseni kwa adani anga, Inu Mulungu wanga, tetezeni kwa anthu ondiwukira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Landitseni kwa adani anga, Inu Mulungu; munditeteze kwa anthu amene auka kutsutsana nane. Onani mutuwo |