Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 55:9 - Buku Lopatulika

9 Aonongeni, Ambuye, gawani lilime lao, pakuti ndaona chiwawa ndi ndeu m'mzindamo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Aonongeni, Ambuye, gawani lilime lao, pakuti ndaona chiwawa ndi ndeu m'mudzimo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Inu Ambuye, onongani zolinga za adani anga, musokoneze upo wao. Pakuti ndikuwona anthu akuchita chiwawa ndi nkhondo mumzindamo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Sokonezani maganizo a oyipa, Inu Ambuye, tsutsani mawu awo; pakuti ine ndikuona chiwawa ndi mkangano mu mzinda.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 55:9
8 Mawu Ofanana  

Ndipo wina anauza Davide nati, Ahitofele ali pakati pa opangana chiwembu pamodzi ndi Abisalomu. Davide nati, Yehova, musandulize uphungu wa Ahitofele ukhale wopusa.


Mwa aneneri a ku Yerusalemu ndinaona chinthu choopsetsa; achita chigololo, ayenda monama, alimbitsa manja a ochita zoipa, ndipo palibe wobwerera kuleka zoipa zake; onse akhala kwa Ine ngati Sodomu, ndi okhalamo ake ngati Gomora.


Monga kasupe atulutsa madzi ake, chomwecho atulutsa zoipa zake; chiwawa ndi kufunkha zimveka m'kati mwake; pamaso panga masiku onse pali kulira ndi mabala.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa