Masalimo 54:6 - Buku Lopatulika6 Ine mwini ndidzapereka nsembe yaufulu kwa Inu, ndidzayamika dzina lanu, Yehova, pakuti nlokoma. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ine mwini ndidzapereka nsembe yaufulu kwa Inu, ndidzayamika dzina lanu, Yehova, pakuti nlokoma. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ndidzapereka nsembe kwa Inu mwaufulu. Ndidzatamanda dzina lanu, Inu Chauta, popeza kuti ndinu abwino. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ine ndidzapereka nsembe yaufulu kwa Inu; ndidzatamanda dzina lanu, Inu Yehova, pakuti ndi labwino. Onani mutuwo |