Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 52:5 - Buku Lopatulika

5 Potero Mulungu adzakupasula kunthawi zonse, adzakuchotsa nadzakukwatula m'hema mwako, nadzakuzula, kukuchotsa m'dziko la amoyo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Potero Mulungu adzakupasula kunthawi zonse, adzakuchotsa nadzakukwatula m'hema mwako, nadzakuzula, kukuchotsa m'dziko la amoyo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Koma Mulungu adzakutswanya kosalekeza, adzakugwira ndi kukutulutsira kunja kwa nyumba yako. Adzakuzula m'dziko la anthu amoyo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Zoonadi Mulungu adzakutsitsa kupita ku chiwonongeko chamuyaya: iye adzakukwatula ndi kukuchotsa mʼtenti yako; iye adzakuzula kuchoka mʼdziko la amoyo.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 52:5
18 Mawu Ofanana  

Adzazulidwa kuhema kwake kumene anakhulupirira; nadzatengedwa kunka naye kwa mfumu ya zoopsa.


Ndidzayenda pamaso pa Yehova m'dziko la amoyo.


Ndikadapanda kukhulupirira kuti ndikaone ubwino wa Yehova m'dziko la amoyo, ndikadatani!


Koma Inu, Mulungu, mudzawatsitsira kudzenje la chionongeko. Anthu okhetsa mwazi ndi achinyengo masiku ao sadzafikira nusu; koma ine ndidzakhulupirira Inu.


Mlomo wa ntheradi ukhazikika nthawi zonse; koma lilime lonama likhala kamphindi.


Mboni yonama sidzakhala yosalangidwa; wolankhula mabodza sadzapulumuka.


Mboni yonama sidzapulumuka chilango; wolankhula mabodza adzaonongeka.


Koma oipa adzalikhidwa m'dziko, achiwembu adzazulidwamo.


Ndipo Ine ndidzakutulutsa iwe mu ntchito yako, ndi kukutsitsa iwe pokhala pako.


Ndinati, Sindidzaona Yehova m'dziko la amoyo; sindidzaonanso munthu pamodzi ndi okhala kunja kuno;


Koma amantha, ndi osakhulupirira, ndi onyansa, ndi ambanda, ndi achigololo, ndi olambira mafano, ndi onse a mabodza, cholandira chao chidzakhala m'nyanja yotentha ndi moto ndi sulufure; ndiyo imfa yachiwiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa