Masalimo 51:3 - Buku Lopatulika3 Chifukwa ndazindikira machimo anga; ndipo choipa changa chili pamaso panga chikhalire. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Chifukwa ndazindikira machimo anga; ndipo choipa changa chili pamaso panga chikhalire. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Zolakwa zanga ndikuzidziŵa, kuchimwa kwanga ndikukuzindikira nthaŵi zonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Pakuti ndikudziwa mphulupulu zanga, ndipo tchimo langa lili pamaso panga nthawi zonse. Onani mutuwo |