Masalimo 50:16 - Buku Lopatulika16 Koma kwa woipa Mulungu anena, Uli nao chiyani malemba anga kulalikira, ndi kutchula pangano langa pakamwa pako? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Koma kwa woipa Mulungu anena, Uli nao chiyani malemba anga kulalikira, ndi kutchula pangano langa pakamwa pako? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Koma kwa munthu woipa Mulungu amati, “Ukuvutikiranji ndi kutchula malamulo anga? Bwanji pakamwa pako pakulankhula za chipangano changa? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Koma kwa woyipa, Mulungu akuti, “Kodi uli ndi mphamvu yanji kuti uzinena malamulo anga kapena kutenga pangano langa pa milomo yako? Onani mutuwo |