Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 50:17 - Buku Lopatulika

17 Popeza udana nacho chilangizo, nufulatira mau anga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Popeza udana nacho chilangizo, nufulatira mau anga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Iwe sufuna kulangizidwa, umaponya mau anga ku nkhongo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Iwe umadana ndi malangizo anga ndipo umaponyera kumbuyo kwako mawu anga.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 50:17
18 Mawu Ofanana  

koma wachimwa koposa onse akale, nukadzipangira milungu ina ndi mafano yoyenga kundikwiyitsa, nunditaya Ine kumbuyo kwako;


Koma anakhala osamvera, napandukira Inu, nataya chilamulo chanu m'mbuyo mwao napha aneneri anu akuwachitira umboni, kuwabwezera kwa Inu, nachita zopeputsa zazikulu.


Kuopa Yehova ndiko chiyambi cha kudziwa; opusa anyoza nzeru ndi mwambo.


Wokonda mwambo akonda kudziwa; koma wakuda chidzudzulo apulukira.


Wosiya njira adzalangidwa mowawa; wakuda chidzudzulo adzafa.


Koma wondichimwira apweteka moyo wake; onse akundida ine akonda imfa.


amene alungamitsa woipa pa chokometsera mlandu, nachotsera wolungama chilungamo chake!


Koma iwo ati, Palibe chiyembekezero; pakuti ife tidzatsata zilingaliro zathu, ndipo tidzachita yense monga mwa kuuma kwa mtima wake woipa.


Anzeru ali ndi manyazi, athedwa nzeru nagwidwa; taonani, akana mau a Yehova; ali nayo nzeru yotani?


ndipo mukakaniza malemba anga, ndi moyo wanu ukanyansidwa nao maweruzo anga, kotero kuti simudzachita malamulo anga onse, koma kuthyola chipangano changa;


Pakuti yense wakuchita zoipa adana nako kuunika, ndipo sakudza kwa kuunika, kuti zingatsutsidwe ntchito zake.


Ndipo monga iwo anakana kukhala naye Mulungu m'chidziwitso chao, anawapereka Mulungu kumtima wokanika, kukachita zinthu zosayenera;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa