Masalimo 50:17 - Buku Lopatulika17 Popeza udana nacho chilangizo, nufulatira mau anga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Popeza udana nacho chilangizo, nufulatira mau anga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Iwe sufuna kulangizidwa, umaponya mau anga ku nkhongo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Iwe umadana ndi malangizo anga ndipo umaponyera kumbuyo kwako mawu anga. Onani mutuwo |