Masalimo 50:12 - Buku Lopatulika12 Ndikamva njala, sindidzakuuza, pakuti dziko lonse ndi langa, ndi kudzala kwake komwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndikamva njala, sindidzakuuza, pakuti dziko lonse ndi langa, ndi kudzala kwake komwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 “Ndikadakhala ndi njala sindikadakuuzani, pakuti dziko lonse ndi zonse zam'menemo, ndi zanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Ndikanakhala ndi njala sindikanakuwuzani, pakuti dziko lonse ndi zonse zimene zili mʼmenemo ndi zanga. Onani mutuwo |