Masalimo 42:10 - Buku Lopatulika10 Adani anga andinyoza ndi kundithyola mafupa anga; pakunena ndine dzuwa lonse, Mulungu wako ali kuti? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Adani anga andinyoza ndi kundithyola mafupa anga; pakunena ndine dzuwa lonse, Mulungu wako ali kuti? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Kunyoza kwa adani anga kumandipweteka ngati bala lofa nalo la m'thupi mwanga, akamandifunsa nthaŵi zonse kuti, “Mulungu wako ali kuti?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Mafupa anga ali ndi ululu wakufa nawo pamene adani anga akundinyoza, tsiku lonse akunena kuti, “Mulungu wako ali kuti?” Onani mutuwo |