Masalimo 37:12 - Buku Lopatulika12 Woipa apangira chiwembu wolungama, namkukutira mano. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Woipa apangira chiwembu wolungama, namkukutira mano. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Munthu woipa amachitira upo mnzake wabwino, namamtuzulira maso mwachidani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Oyipa amakonza chiwembu kutsutsana ndi olungama ndipo amawakukutira mano; Onani mutuwo |