Masalimo 32:7 - Buku Lopatulika7 Inu ndinu mobisalira mwanga; m'nsautso mudzandisunga; mudzandizinga ndi nyimbo za chipulumutso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Inu ndinu mobisalira mwanga; m'nsautso mudzandisunga; mudzandizinga ndi nyimbo za chipulumutso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Inu ndinu kobisalira kwanga. Inu mumanditchinjiriza nthaŵi yamavuto. Nchifukwa chake ndimaimba nyimbo zotamanda chipulumutso chanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Inu ndi malo anga obisala; muzinditeteza ku mavuto ndipo muzindizinga ndi nyimbo zachipulumutso. Sela Onani mutuwo |