Masalimo 31:4 - Buku Lopatulika4 Mundionjole mu ukonde umene ananditchera mobisika. Pakuti Inu ndinu mphamvu yanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Mundionjole m'ukonde umene ananditchera mobisika. Pakuti Inu ndinu mphamvu yanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Onjoleni mu ukonde umene anditchera, pakuti Inu ndinu pothaŵira panga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ndimasuleni mu msampha umene anditchera pakuti ndinu pothawirapo panga. Onani mutuwo |