Masalimo 31:5 - Buku Lopatulika5 Ndipereka mzimu wanga m'dzanja lanu; mwandiombola, Inu Yehova, Mulungu wa choonadi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipereka mzimu wanga m'dzanja lanu; mwandiombola, Inu Yehova, Mulungu wa choonadi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ndikupereka moyo wanga m'manja mwanu. Inu Chauta wokhulupirika, mwandiwombola. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Mʼmanja mwanu ndipereka mzimu wanga; womboleni Yehova Mulungu wachoonadi. Onani mutuwo |
Chifukwa chanji ndinafika osapeza munthu? Ndi kuitana koma panalibe wina woyankha? Kodi dzanja langa lafupika konse, kuti silingathe kuombola? Pena Ine kodi ndilibe mphamvu zakupulumutsa? Taona pa kudzudzula kwanga ndiumitsa nyanja, ndi kusandutsa mitsinje chipululu; nsomba zake zinunkha chifukwa mulibe madzi, ndipo zifa ndi ludzu.