Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 29:4 - Buku Lopatulika

4 Liu la Yehova ndi lamphamvu; liu la Yehova ndi lalikulukulu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Liu la Yehova ndi lamphamvu; liu la Yehova ndi lalikulukulu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Liwu la Chauta ndi lamphamvu, liwu la Chauta ndi laulamuliro.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Liwu la Yehova ndi lamphamvu; liwu la Yehova ndi laulemerero.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 29:4
13 Mawu Ofanana  

Pakuti ananena, ndipo chinachitidwa; analamulira, ndipo chinakhazikika.


Kwa Iye wakuberekeka pamwambamwamba, oyambira kale lomwe; taonani; amveketsa liu lake, ndilo liu lamphamvu.


Vomerezani kuti mphamvu nja Mulungu; ukulu wake uli pa Israele, ndi mphamvu yake m'mitambo.


Yehova Wam'mwamba ndiye wamphamvu, wakuposa mkokomo wa madzi ambiri, ndi mafunde olimba a nyanja.


Ndipo Yehova adzamveketsa mau ake a ulemerero, ndipo adzaonetsa kumenya kwa dzanja lake, ndi mkwiyo wake waukali, ndi lawi la moto wonyambita, ndi kuomba kwa mphepo, ndi mkuntho ndi matalala.


Mau a phokoso achokera m'mzinda, mau ochokera mu Kachisi, mau a Yehova amene abwezera adani ake chilango.


Ndipo mkokomo wa mapiko a akerubi unamveka mpaka bwalo lakunja, ngati mau a Mulungu Wamphamvuyonse, pakunena Iye.


Ndipo anati, Yehova adzadzuma ali mu Ziyoni, nadzamveketsa mau ake ali mu Yerusalemu; podyetsa abusa padzachita chisoni, ndi mutu wa Karimele udzauma.


Ndipo anthu onse anadabwa, nalankhulana wina ndi mnzake, nanena, Mau amenewa ali otani? Chifukwa ndi ulamuliro ndi mphamvu angolamulira mizimu yonyansa, ndipo ingotuluka.


Ndipo Iye anati kwa iwo, Chikhulupiriro chanu chili kuti? Ndipo m'kuchita mantha anazizwa iwo, nanena wina ndi mnzake, Uyu ndani nanga, kuti angolamula mphepo ndi madzi, ndipo zimvera Iye?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa