Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 29:5 - Buku Lopatulika

5 Liu la Yehova lithyola mitengo yamkungudza; inde Yehova athyola mikungudza ya ku Lebanoni.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Liu la Yehova lithyola mitengo yamkungudza; inde Yehova athyola mikungudza ya ku Lebanoni.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Liwu la Chauta limathyola mikungudza, Chauta amathyolathyoladi mikungudza ya ku Lebanoni.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Liwu la Yehova limathyola mikungudza; Yehova amathyolathyola mikungudza ya ku Lebanoni.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 29:5
3 Mawu Ofanana  

Mitengo ya Yehova yadzala ndi madzi; mikungudza ya ku Lebanoni imene anaioka;


ndi pa mitengo yonse yamkungudza ya Lebanoni, yaitali ndi yotukulidwa, ndi pa mitengo yonse yathundu ya Basani;


Ndipo nkandankhuku unati kwa mitengo, Mukandidzoza mfumu yanu moonadi, tiyeni, thawirani ku mthunzi wanga; mukapanda kutero utuluke moto m'nkandankhuku ndi kunyeketsa mikungudza ya Lebanoni.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa