Masalimo 27:8 - Buku Lopatulika8 Pamene munati, Funani nkhope yanga; mtima wanga unati kwa Inu. Nkhope yanu, Yehova, ndidzaifuna. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Pamene munati, Funani nkhope yanga; mtima wanga unati kwa Inu. Nkhope yanu, Yehova, ndidzaifuna. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Pajatu Inu mudati, “Muzifunafuna nkhope yanga.” Inu Chauta, ndidzafunafuna nkhope yanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Mtima wanga ukuti kwa Inu, “Funafuna nkhope yake!” Nkhope yanu Yehova ndidzayifunafuna. Onani mutuwo |