Masalimo 25:9 - Buku Lopatulika9 Adzawatsogolera ofatsa m'chiweruzo; ndipo adzaphunzitsa ofatsa njira yake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Adzawatsogolera ofatsa m'chiweruzo; ndipo adzaphunzitsa ofatsa njira yake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Amatsogolera anthu odzichepetsa kuti achite zolungama, amaŵaphunzitsa njira zake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Amatsogolera odzichepetsa kuti achite zolungama ndipo amawaphunzitsa njira zake. Onani mutuwo |