Masalimo 20:8 - Buku Lopatulika8 Iwowa anagonjeka, nagwa; koma ife tauka, ndipo takhala chilili. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Iwowa anagonjeka, nagwa; koma ife tauka, ndipo takhala chilili. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Adani adzaphofomoka ndi kugwa, koma ife tidzadzuka kukhala chilili. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Iwo amagonjetsedwa ndi kugwa, koma ife timadzuka ndi kuyima chilili. Onani mutuwo |