Masalimo 20:6 - Buku Lopatulika6 Tsopano ndidziwa kuti Yehova apulumutsa wodzozedwa wake; adzamvomereza mu Mwamba mwake moyera ndi mphamvu ya chipulumutso cha dzanja lake lamanja. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Tsopano ndidziwa kuti Yehova apulumutsa wodzozedwa wake; adzamvomereza m'Mwamba mwake moyera ndi mphamvu ya chipulumutso cha dzanja lake lamanja. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Tsopano ndikudziŵa kuti Chauta adzathandiza wodzozedwa wake. Adzamuyankha ali ku malo ake oyera kumwamba, pakumpambanitsa kwathunthu ndi dzanja lake lamanja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Tsopano ndadziwa kuti Yehova amapulumutsa wodzozedwa wake; Iye amamuyankha kuchokera kumwamba ku malo ake opatulika ndi mphamvu yopulumutsa ya dzanja lake lamanja. Onani mutuwo |