Masalimo 20:1 - Buku Lopatulika1 Yehova akuvomereze tsiku la nsautso; dzina la Mulungu wa Yakobo likuike pamsanje; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Yehova akuvomereze tsiku la nsautso; dzina la Mulungu wa Yakobo likuike pamsanje; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Chauta akuthandize pa tsiku lamavuto. Mulungu wa Yakobe akuteteze. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Yehova akuyankhe pamene uli pa msautso; dzina la Mulungu wa Yakobo likuteteze. Onani mutuwo |