Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 144:3 - Buku Lopatulika

3 Yehova, munthu ndani kuti mumdziwa? Mwana wa munthu kuti mumsamalira?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Yehova, munthu ndani kuti mumdziwa? Mwana wa munthu kuti mumsamalira?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Inu Chauta, kodi munthu nchiyani, kuti muzimsamala? Mwana wa munthu nchiyani, kuti muzimganizira?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Inu Yehova, munthu nʼchiyani kuti mumamusamalira, mwana wa munthu kuti muzimuganizira?

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 144:3
7 Mawu Ofanana  

Munthu nchiyani kuti akhale woyera, wobadwa ndi mkazi kuti akhale wolungama?


Munthu ndani kuti mumkuze, ndi kuti muike mtima wanu pa iye,


munthu ndani kuti mumkumbukira? Ndi mwana wa munthu kuti mucheza naye?


Pakuti munamchepsa pang'ono ndi Mulungu, munamveka iye korona wa ulemerero ndi ulemu.


Siyani munthu, amene mpweya wake uli m'mphuno mwake; chifukwa m'mene awerengedwamo ndi muti?


Koma wina anachita umboni pena, nati, Munthu nchiyani kuti mumkumbukira iye? Kapena mwana wa munthu kuti mucheza naye?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa