Masalimo 139:7 - Buku Lopatulika7 Ndidzapita kuti kuzembera mzimu wanu? Kapena ndidzathawira kuti kuzembera nkhope yanu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndidzapita kuti kuzembera mzimu wanu? Kapena ndidzathawira kuti kuzembera nkhope yanu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Ndidzapita kuti, pofuna kupewa Mzimu wanu, kapena pofuna kuthaŵa nkhope yanu? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Kodi ndingapite kuti kufuna kuzemba Mzimu wanu? Kodi ndingathawire kuti kuchoka pamaso panu? Onani mutuwo |