Masalimo 139:21 - Buku Lopatulika21 Kodi sindidana nao iwo akudana ndi Inu, Yehova? Ndipo kodi sindimva nao chisoni iwo akuukira Inu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Kodi sindidana nao iwo akudana ndi Inu, Yehova? Ndipo kodi sindimva nao chisoni iwo akuukira Inu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Kodi sindidana nawo anthu odana nanu, Inu Chauta? Kodi sindinyansidwa nawo anthu okuukirani? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Kodi ine sindidana nawo amene amakudani, Inu Yehova? Kodi sindinyansidwa nawo amene amakuwukirani? Onani mutuwo |