Masalimo 139:19 - Buku Lopatulika19 Indedi, mudzaomba woipa, Mulungu: Ndipo amuna inu okhumba mwazi, chokani kwa ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Indedi, mudzaomba woipa, Mulungu: Ndipo amuna inu okhumba mwazi, chokani kwa ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Ndikadakonda kuti muwononge anthu oipa, Inu Mulungu, ndipo kuti anthu okhetsa magazi andichokere. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Ndi bwino mukanangopha anthu oyipa, Inu Mulungu! Chokereni inu anthu owononga anzanu! Onani mutuwo |