Masalimo 139:17 - Buku Lopatulika17 Potero, Mulungu, ndiziyesa zolingalira zanu za mtengo wake ndithu! Mawerengedwe ake ndi ambirimbiri! Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Potero, Mulungu, ndiziyesa zolingalira zanu za mtengo wake ndithu! Mawerengedwe ake ndi ambirimbiri! Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Maganizo anu, Inu Mulungu, ndi ozama kwa ine, ndi osaŵerengeka konse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Zolingalira zanu pa ine ndi zamtengowapatali, Inu Mulungu, ndi zosawerengeka ndithu! Onani mutuwo |