Masalimo 139:13 - Buku Lopatulika13 Pakuti Inu munalenga impso zanga; munandiumba ndisanabadwe ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Pakuti Inu munalenga impso zanga; munandiumba ndisanabadwe ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Paja ndinu mudapanga za m'kati mwanga, mudandiwumba m'mimba mwa amai anga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Pakuti Inu munalenga za mʼkati mwanga; munandiwumba pamodzi mʼmimba mwa amayi anga. Onani mutuwo |