Masalimo 132:6 - Buku Lopatulika6 Taonani, tinachimva mu Efurata; tinachipeza kuchidikha cha kunkhalango. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Taonani, tinachimva m'Efurata; tinachipeza kuchidikha cha kunkhalango. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Tidamva za bokosi lachipangano ku Efurata, tidalipeza m'minda ya ku Yaara. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Zoonadi, tinamva za Bokosi la Chipangano ku Efurata, tinalipeza mʼminda ya ku Yaara: Onani mutuwo |