Masalimo 119:5 - Buku Lopatulika5 Ha? Mwenzi zitakhazikika njira zanga kuti ndisamalire malemba anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ha? Mwenzi zitakhazikika njira zanga kuti ndisamalire malemba anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ndikadakonda kuti njira zanga zikhale zokhulupirika, pakumvera malamulo anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Aa! Ndikanakonda njira zanga zikanakhala zokhazikika pa kumvera zophunzitsa zanu! Onani mutuwo |