Masalimo 119:170 - Buku Lopatulika170 Kupemba kwanga kudze pamaso panu; mundilanditse monga mwa mau anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 2014170 Kupemba kwanga kudze pamaso panu; mundilanditse monga mwa mau anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa170 Kupempha kwanga kumveke kwa Inu. Mundipulumutse potsata malonjezo anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero170 Kupempha kwanga kufike pamaso panu; pulumutseni molingana ndi lonjezo lanu. Onani mutuwo |