Masalimo 119:171 - Buku Lopatulika171 Milomo yanga itulutse chilemekezo; popeza mundiphunzitsa malemba anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 2014171 Milomo yanga itulutse chilemekezo; popeza mundiphunzitsa malemba anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa171 Pakamwa panga padzakutamandani, chifukwa mumandiphunzitsa malamulo anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero171 Matamando asefukire pa milomo yanga, pakuti Inu mumandiphunzitsa malamulo anu. Onani mutuwo |