Masalimo 109:2 - Buku Lopatulika2 pakuti pakamwa pa woipa ndi pakamwa pa chinyengo pananditsegukira; anandilankhulira ndi m'kamwa mwa bodza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 pakuti pakamwa pa woipa ndi pakamwa pa chinyengo pananditsegukira; anandilankhulira ndi m'kamwa mwa bodza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 pakuti anthu oipa ndi onama amakamba zondiwukira, amalankhula zondinamizira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 pakuti anthu oyipa ndi achinyengo atsekula pakamwa pawo kutsutsana nane; iwo ayankhula motsutsana nane ndi malilime abodza. Onani mutuwo |