Masalimo 106:3 - Buku Lopatulika3 Odala iwo amene asunga chiweruzo, iye amene achita chilungamo nthawi zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Odala iwo amene asunga chiweruzo, iye amene achita chilungamo nthawi zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Ngodala anthu otsata malamulo a Chauta, anthu ochita zolungama nthaŵi zonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Odala ndi amene amasunga chilungamo, amene amachita zolungama nthawi zonse. Onani mutuwo |