Masalimo 106:4 - Buku Lopatulika4 Mundikumbukire, Yehova, monga momwe muvomerezana ndi anthu anu; mundionetsa chipulumutso chanu: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Mundikumbukire, Yehova, monga momwe muvomerezana ndi anthu anu; mundionetsa chipulumutso chanu: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Chauta, mundikumbukire pamene mukukomera mtima anthu anu. Mundithandize pamene mukuŵapulumutsa, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Mundikumbukire Yehova, pamene mukuonetsa kukoma mtima kwanu kwa anthu anu, bwerani mudzandithandize pamene mukuwapulumutsa iwo, Onani mutuwo |