Masalimo 103:18 - Buku Lopatulika18 kwa iwo akusunga chipangano chake, ndi kwa iwo akukumbukira malangizo ake kuwachita. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 kwa iwo akusunga chipangano chake, ndi kwa iwo akukumbukira malangizo ake kuwachita. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Anthuwo ndi amene amasunga chipangano chake, amene amakumbukira kusunga malamulo ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 iwo amene amasunga pangano lake ndi kukumbukira kumvera malangizo ake. Onani mutuwo |