Masalimo 103:14 - Buku Lopatulika14 Popeza adziwa mapangidwe athu; akumbukira kuti ife ndife fumbi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Popeza adziwa mapangidwe athu; akumbukira kuti ife ndife fumbi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Amadziŵa m'mene adatipangira, amakumbukira kuti ife ndife fumbi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 pakuti Iye amadziwa momwe tinawumbidwira, amakumbukira kuti ndife fumbi. Onani mutuwo |