Masalimo 103:15 - Buku Lopatulika15 Koma munthu, masiku ake akunga udzu; aphuka monga duwa lakuthengo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Koma munthu, masiku ake akunga udzu; aphuka monga duwa la kuthengo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Kunena za munthu, masiku ake sakhalitsa, ali ngati a udzu, munthuyo amakondwa ngati duŵa lakuthengo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Kunena za munthu, masiku ake ali ngati udzu, amaphuka ngati duwa la mʼmunda; Onani mutuwo |