Masalimo 103:12 - Buku Lopatulika12 Monga kum'mawa kutanimpha ndi kumadzulo, momwemo anatisiyanitsira kutali zolakwa zathu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Monga kum'mawa kutanimpha ndi kumadzulo, momwemo anatisiyanitsira kutali zolakwa zathu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Monga kuvuma kuli kutali ndi kuzambwe, ndi momwenso amachotsera zolakwa zathu kuti zikhale kutali ndi ife. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 monga kummawa kutalikirana ndi kumadzulo, koteronso Iye watichotsera mphulupulu zathu kuti zikhale kutali nafe. Onani mutuwo |