Masalimo 10:13 - Buku Lopatulika13 Woipa anyozeranji Mulungu, anena m'mtima mwake, Simudzafunsira? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Woipa anyozeranji Mulungu, anena m'mtima mwake, Simudzafunsira? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Chifukwa chiyani munthu woipa amanyoza Mulungu? Chifukwa chiyani mumtima mwake amati, “Sadzandilanga?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Nʼchifukwa chiyani munthu woyipa amachitira chipongwe Mulungu? Chifukwa chiyani amati mu mtima mwake, “Iye sandiyimba mlandu?” Onani mutuwo |